Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 96:9-11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. Gwadirani Yehova moyera ndi mokometsetsa:Njenjemerani pamaso pace, inu dziko lonse lapansi.

10. Nenani mwa amitundu, Yehova acita ufumu;Dziko lokhalamo anthu lomwe likhazikika kuti silingagwedezeke;Adzaweruza mitundu ya anthu molunjika.

11. Kumwamba kukondwere nilisekerere dziko lapansi;Nyanja ibume mwa kudzala kwace:

Werengani mutu wathunthu Masalmo 96