13. Kuti mumpumitse masiku oipa;Kufikira atakumbira woipa mbuna.
14. Pakuti Yehova sadzasiya anthu ace,Ndipo sadzataya colandira cace.
15. Pakuti ciweruzo cidzabwera kumka kucilungamo:Ndipo oongoka mtima onse adzacitsata.
16. Adzandiukira ndani kutsutsana nao ocita zoipa?Adzandilimbikira ndani kutsutsana nao ocita zopanda pace?
17. Akadapanda kukhala thandizo langa Yehova,Moyo wanga ukadakhala kuli cete.