Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 91:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Iye amene akhala pansi m'ngaka yace ya Wam'mwambamwambaAdzagonera mu mthunzi wa Wamphamvuyonse.

2. Ndidzati kwa Yehova, Pothawirapo panga ndi linga langa;Mulungu wanga, amene ndimkhulupirira,

3. Pakuti adzakuonjola ku msampha wa msodzi,Ku mliri wosakaza.

4. Adzakufungatira ndi nthenga zace,Ndipo udzathawira kunsi kwa mapiko ace;Coonadi cace ndico cikopa cocinjiriza.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 91