17. Oipawo adzabwerera kumanda,Inde amitundu onse akuiwala Mulungu.
18. Pakuti sadzaiwalika nthawi zonse waumphawi,Kapena ciyembekezo ca ozunzika sicidzaonongeka kosatha.
19. Ukani, Yehova, asalimbike munthu;Amitundu aweruzidwe pankhope panu.
20. Muwacititse mantha, Yehova; Adziwe amitundu kuti ali anthu.