15. Wozunzika ine ndi wofuna kufa kuyambira ubwana wanga;Posenza zoopsa zanu, ndithedwa nzeru.
16. Kuzaza kwanu kwandimiza;Zoopsa zanu zinandiononga,
17. Zinandizungulira ngati madzi tsiku lonse;Zinandizinga pamodzi.
18. Munandicotsera kutali wondikonda ndi bwenzi langa,Odziwana nane akhala kumdima.