6. Munamcititsa ufumu pa nchito za manja anu;Mudagonjetsa zonse pansi pa mapazi ace;
7. Nkhosa ndi ng'ombe, zonsezo,Ndi nyama za kuthengo zomwe;
8. Mbalame za m'mlengalenga, ndi nsomba za m'nyanja.Zopita m'njira za m'nyanja.
9. Yehova, Ambuye wathu,Dzina lanu liposadi nanga pa dziko lonse lapansi!