Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 76:6-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Pa kudzudzula kwanu, Mulungu wa Yakobo,Gareta ndi kavalo yemwe anagwa m'tulo.

7. Inu ndinu woopsa;Ndipo utauka mkwiyo wanu adzakhala ciriri ndani pamaso panu?

8. Mudamveketsa ciweruzo cocokera Kumwamba;Dziko lapansi linacita mantha, nilinakhala cete,

9. Pakuuka Mulungu kuti aweruze,Kuti apulumutse ofatsa onse a pa dziko lapansi.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 76