1. Mulungu adziwika mwa Yuda:Dzina lace limveka mwa Israyeli.
2. Msasa wace unali m'Salemu, Ndipo pokhala Iye m'Ziyoni.
3. Pomwepo anatyola mibvi ya paota;Cikopa, ndi lupanga, ndi nkhondo.
4. Inu ndinu wakuunikira, ndi womveka wakuposa mapiri muli acifwamba.