Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 72:3-7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Mapiri adzatengera anthu mtendere,Timapiri tomwe, m'cilungamo.

4. Adzaweruza ozunzika a mwa anthu,Adzapulumutsa ana aumphawi,Nadzaphwanya wosautsa.

5. Adzakuopani momwe likhalira dzuwa ndi mwezi,Kufikira mibadwo mibadwo.

6. Adzanga mvula yakugwa pa udzu wosenga:Monga mvula yothirira dziko.

7. Masiku ace wolungama adzakhazikika;Ndi mtendere wocuruka, kufikira sipadzakhala mwezi.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 72