8. Cokani kwa ine, nonsenu akucita zopanda pace;Pakuti wamva Yehova mau a kulira kwanaa,
9. Wamva Yehova kupemba kwanga;Yehova adzalandira pemphero langa.
10. Adzacita manyazi, nadzanthunthumira kwakukuru adani anga onse;Adzabwerera, nadzacita manyazi modzidzimuka,