Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 6:8-10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

8. Cokani kwa ine, nonsenu akucita zopanda pace;Pakuti wamva Yehova mau a kulira kwanaa,

9. Wamva Yehova kupemba kwanga;Yehova adzalandira pemphero langa.

10. Adzacita manyazi, nadzanthunthumira kwakukuru adani anga onse;Adzabwerera, nadzacita manyazi modzidzimuka,

Werengani mutu wathunthu Masalmo 6