Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 53:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Citsiru cimati mumtima mwace, Kulibe Mulungu.Acita zobvunda, acita cosalungama conyansa;Kulibe wakucita bwino.

2. Mulungu m'mwamba anaweramira pa ana a anthu,Kuti aone ngati aliko wanzeru, Wakufuna Mulungu.

3. Onse anabwerera; anabvunda mtima pamodzi;Palibe mmodzi wakucita bwino, nnena mmodzi.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 53