8. Idzani, penyani nchito za Yehova,Amene acita zopululutsa pa dziko lapansi.
9. Aletsa nkhondo ku malekezero adziko lapansi;Athyola uta, nadula nthungo;Atentha magareta ndi moto.
10. Khalani cete, ndipo dziwani kuti Ine ndine Mulungu:Ndidzabuka mwa amitundu,Ndidzabuka pa dziko lapansi.
11. Yehova wa makamu ali ndi ife,Mulungu wa Yakobo ndiye pamsanje pathu,