Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 39:11-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. Pamene mulanga munthu ndi zomdzudzula cifukwa ca mphulupulu,Mukanganula kukongola kwace monga mumacita ndi kadzoce:Indedi, munthu ali yense ali cabe.

12. Imvani pemphero langa, Yehova, ndipo cherani khutu kulira kwanga;Musakhale cete pa misozi yanga:Pakuti ine ndine mlendo ndi Inu,Wosakhazikika, monga makolo anga onse.

13. Ndiloleni, kuti nditsitsimuke,Ndisanamuke ndi kukhala kuli zi.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 39