Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 38:19-22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

19. Koma adani anga ali ndi moyo, nakhalandi mphamvu:Ndipo akundida kopanda cifukwa acuruka.

20. Ndipo iwo akubwezera coipa pa cabwinoAtsutsana nane, popeza nditsata cabwino.

21. Musanditaye, Yehova:Mulungu wanga, musakhale kutali ndi ine.

22. Fulumirani kundithandiza,Ambuye, cipulumutso canga.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 38