Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 34:16-22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. Nkhopeya Yehovaitsutsananao akucita zoipa,Kudula cikumbukilo cao pa dziko lapansi.

17. Iwowo anaitana, ndipo Yehova anawamva,Nawalanditsa ku masautso ao onse.

18. Yehova ali pafupi ndi iwo a mtimawosweka,Apulumutsa iwo a mzimu wolapadi,

19. Masautso a wolungama mtima acuruka:Koma Yehova amlanditsa mwa onsewa.

20. Iye asunga mafupa ace onse:Silinatyoka limodzi lonse.

21. Mphulupulu idzamupha woipa:Ndipo adzawatsutsa kumlandu iwo akudana naye wolungama.

22. Yehova aombola moyo wa anyamata ace,Ndipo sadzawatsutsa kumlandu onse akukhulupirira Iye.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 34