12. Munthu wokhumba moyo ndani,Wokonda masiku, kuti aone zabwino?
13. Uletse lilime lako lisachule zoipa,Ndipo milomo yako isalankhule cinyengo.
14. Pfutuka pazoipa, nucite zabwino,Funa mtendere ndi kuulondola.
15. Maso a Yehova ali pa olungama mtima,Ndipo makutu ace achereza kulira kwao.