Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 34:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndidzalemekeza Yehova nyengo zonse;Kumlemekeza kwace kudzakhala m'kamwa mwanga kosalekeza.

2. Moyo wanga udzatamanda Yehova;Ofatsa adzakumva nadzakondwera.

3. Bukitsani pamodzi ndine ukuru wa Yehova,Ndipo tikweze dzina lace pamodzi.

4. Ndinafuna Yehova ndipo anandibvomera,Nandlianditsa m'mantha anga Onse.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 34