Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 2:3-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Tidule zomangira zao,Titaye nsinga zao.

4. Wokhala m'mwambayo adzaseka;Ambuye adzawanyoza.

5. Pomwepo adzalankhula nao mu mkwiyo wace,Nadzawaopsa m'ukali wace:

6. Koma Ine ndadzoza mfumu yangaPa Ziyoni, phiri langa loyera.

7. Ndidzauza za citsimikizo:Yehova ananena ndiIne, Iwe ndiwe Mwana wanga;Ine lero ndakubala.

8. Undifunse, ndipo ndidzakupatsa amitundu akhale colowa cako,Ndi malekezero a dziko lapansi akhale ako ako.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 2