Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 18:12-15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

12. Mwa kucezemira kunali pamaso pace makongwa anakanganuka,Matalala ndi makala amoto.

13. Ndipo anagunda m'mwamba Yehova,Ndipo Wam'mwambamwamba anamvetsa liu lace;Matalala ndi makala amoto,

14. Ndipo anatuma mibvi yace nawabalalitsa;Inde mphezi zaunyinji, nawamwaza.

15. Ndipo zidaoneka zoyendamo madzi,Nafukuka maziko a dziko lapansi,Mwa kudzudzula kwanu, Yehova,Mwa mpumo wa mpweya wa m'mphuno mwanu.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 18