Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 16:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndisungeni ine, Mulungu: pakuti ndakhulupirira Inu.

2. Ndinati kwa Yehova, Inu ndinu Ambuye wanga:Ndiribe cabwino cina coposa Inu.

3. Za oyera mtima okhala pa dziko lapansi,Iwo ndiwo omveka mbiri, mwa iwowo muli cikondwero canga conse.

4. Zidzacuruka zisoni zao za iwo otsata mulungu wina:Sindidzathira nsembe zao zamwazi,Ndipo sindidzachula maina ao pakamwa panga,

Werengani mutu wathunthu Masalmo 16