Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 148:11-14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. Mafumu a padziko ndi mitundu yonse ya anthu;Zinduna ndi oweruza onse a padziko;

12. Anyamata ndiponso anamwali;Okalamba pamodzi ndi ana:

13. Alemekeze dzina la Yehova;Pakuti dzina lace lokha ndi lokwezeka;Ulemerero wace uli pamwamba pa dziko lapansi ndi thambo.

14. Ndipo anakweza nyanga ya anthu ace,Cilemekezo ca okondedwa ace onse;Ndiwo ana a Israyeli, anthu a pafupi pa Iye,Haleluya,

Werengani mutu wathunthu Masalmo 148