1. Ndipfuula nalo liu langa kwa Yehova;Ndi mau anga ndipemba kwa Yehova.
2. Nditsanulirakudandaulakwanga pamaso pace;Ndionetsa msauko wanga pamaso pace.
3. Pamene mzimu wanga unakomoka m'kati mwanga, munadziwa njira yanga.M'njira ndiyendamo anandichera msampha,
4. Penyani ku dzanja lamanja ndipo muone; palibe wondidziwa;Pothawirapo pandisowa; palibe mmodzi wosamalira moyo wanga.
5. Ndinapfuulira kwa inu, Yehova;Ndina, Inu ndinu pothawirapo panga,Gawo langa m'dziko la amoyo.