11. Munthu wamlomo sadzakhazikika pa dziko lapansi;Coipa cidzamsaka munthu waciwawa kuti cimgwetse.
12. Ndidziwa kuti Yehova adzanenera wozunzika mlandu,Ndi kuweruzira aumphawi,
13. Indedi, olungama adzayamika dzina lanu;Oongoka mtima adzakhala pamaso panu,