6. Lilime langa limamatike ku nsaya zanga,Ndikapanda kukumbukila inu;Ndikapanda kusankha YerusalemuKoposa cimwemwe canga copambana.
7. Yehova, kumbukilani ana a EdomuTsiku la Yerusalemu;Amene adati, Gamulani, gamulani,Kufikira maziko ace.
8. Mwana wamkazi wa ku Babulo, iwe amene udzapasulidwa;Wodala iye amene adzakubwezera cilangoMonga umo unaticitira ife.
9. Wodala iye amene adzagwira makanda ako,Ndi kuwaphwanya pathanthwe.