Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 137:6-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Lilime langa limamatike ku nsaya zanga,Ndikapanda kukumbukila inu;Ndikapanda kusankha YerusalemuKoposa cimwemwe canga copambana.

7. Yehova, kumbukilani ana a EdomuTsiku la Yerusalemu;Amene adati, Gamulani, gamulani,Kufikira maziko ace.

8. Mwana wamkazi wa ku Babulo, iwe amene udzapasulidwa;Wodala iye amene adzakubwezera cilangoMonga umo unaticitira ife.

9. Wodala iye amene adzagwira makanda ako,Ndi kuwaphwanya pathanthwe.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 137