Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 136:17-24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

17. Amene anapanda mafumu akulu:Pakuti cifundo cace ncosatha,

18. Ndipo anawapha mafumu omveka:Pakuti cifundo cace ncosatha.

19. Sihoni mfumu ya Aamori;Pakuti cifundo cace ncosatha.

20. Ndi ogi mfumu ya Basana:Pakuti cifundo cace ncosatha.

21. Ndipo anaperekadzikolaolikhale cosiyira;Pakuti cifundo cace ncosatha.

22. Cosiyira ca kwa Israyeli mtumiki wace;Pakuti cifundo cace ncosatha.

23. Amene anatikumbukila popepuka ife;Pakuti cifundo cace ncosatha.

24. Natikwatula kwa otisautsa;Pakuti cifundo cace ncosatha.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 136