1. Yamikani Yehova pakuti ndiye wabwino:Pakuti cifundo cace ncosatha.
2. Yamikani Mulungu wa milungu:Pakuti cifundo cace ncosatha.
3. Yamikani Mbuye wa ambuye:Pakuti cifundo cace ncosatha.
4. Amene yekha acita zodabwiza zazikuru:Pakuti cifundo cace ncosatha.
5. Amene analenga zakumwamba mwanzeru:Pakuti cifundo cace ncosatha.