Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 136:1-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Yamikani Yehova pakuti ndiye wabwino:Pakuti cifundo cace ncosatha.

2. Yamikani Mulungu wa milungu:Pakuti cifundo cace ncosatha.

3. Yamikani Mbuye wa ambuye:Pakuti cifundo cace ncosatha.

4. Amene yekha acita zodabwiza zazikuru:Pakuti cifundo cace ncosatha.

5. Amene analenga zakumwamba mwanzeru:Pakuti cifundo cace ncosatha.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 136