13. Pakuti Yehova anasankha Ziyoni;Analikhumba likhale pokhala pace; ndi kuti,
14. Pampumulo panga mpano posatha:Pano ndidzakhala; pakuti ndakhumbapo.
15. Ndidzadalitsatu cakudya cace;Aumphawi ace ndidzawakhutitsa ndi mkate.
16. Ndipo ansembe ace ndidzawabveka ndi cipulumutso:Ndi okondedwa ace adzapfuulitsa mokondwera.
17. Apo ndidzaphukitsira Davide nyanga;Ndak onzeraru wodzozedwa wanga nyali.
18. Ndidzawabvekaadani ace ndi manyaziKoma pa iyeyu korona wace adzambveka.