Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 129:1-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Anandisautsa kawiri kawiri kuyambira ubwana wanga,Anene tsono Israyeli;

2. Anandisautsa kawiri kawiri kuyambira ubwana wanga;Koma sanandilaka.

3. Olima analima pamsana panga;Anatalikitsa mipere yao.

4. Yehova ndiye wolungama;Anadulatu zingwe za oipa.

5. Acite manyazi nabwerere m'mbuyo.Onse akudana naye Ziyoni.

6. Akhale ngati udzu womera patsindwi,Wakufota asanauzule;

Werengani mutu wathunthu Masalmo 129