Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 126:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo pakamwa pathu panadzala ndi kuseka,Ndi lilime lathu linapfuula mokondwera;Pamenepo anati mwa amitundu,Yehova anawacitira iwo zazikuru,

Werengani mutu wathunthu Masalmo 126

Onani Masalmo 126:2 nkhani