Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 118:22-26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

22. Mwala umene omangawo anaukanaWakhala mutu wa pangondya.

23. Ici cidzera kwa Yehova;Ncodabwiza ici pamaso pathu.

24. Tsiku ili ndilo adaliika Yehova;Tidzasekera ndi kukondwera m'mwemo.

25. Tikupemphani, Yehova, tipulumutseni tsopano;Tikupemphani, Yehova, tipindulitseni tsopano.

26. Wodala wakudzayo m'dzina la Yehova;Takudalitsani kocokera m'nyumba ya Yehova.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 118