11. Adandizinga, inde, adandizinga:Indedi, m'dzinala Yehova ndidzawaduladula.
12. Adandizinga ngati njuci;Anazima ngati moto waminga;Indedi, m'dzina la Yehova ndidzawaduladula.
13. Kundikankha anandikankha ndikadagwa;Koma Yehova anandithandiza.
14. Yehova ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga;Ndipo anakhala cipulumutso canga.