7. Pa kudzudzula kwanu anathawa;Anathawa msanga liu la bingu lanu;
8. Anakwera m'mapiri, anatsikira m'zigwa,Kufikira malo mudawakonzeratu.
9. Munaika malire kuti asapitirireko;Kuti asabwererenso kuphimba dziko lapansi.
10. Atumiza akasupe alowe m'makwawa;Ayenda pakati pa mapiri:
11. Zimamwamo nyama zonse za kuthengo;Mbidzi zipherako ludzu lao.
12. Mbalame za mlengalenga zifatsa pamenepo,Zimayimba pakati pa mitawi.