Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 103:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma cifundo ca Yehova ndico coyambira nthawi yosayamba kufikira nthawi yosatha kwa iwo akumuopa Iye,Ndi cilungamo cace kufikira kwa ana a ana;

Werengani mutu wathunthu Masalmo 103

Onani Masalmo 103:17 nkhani