18. Pa phiri la Ziyoni lopasukaloAnkhandwe ayendapo.
19. Inu, Yehova, mukhala cikhalire,Ndi mpando wanu wacifumu ku mibadwo mibadwo.
20. Bwanji mutiiwala ciiwalire,Ndi kutisiya masiku ambirimbiri;
21. Mutitembenuzire kwa Inu, Yehova, ndipo tidzatembenuzidwadi,Mukonzenso masiku athu ngati kale lija.
22. Koma mwatikaniza konse,Mwatikwiyira kopambana.