Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Maliro 5:18-22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

18. Pa phiri la Ziyoni lopasukaloAnkhandwe ayendapo.

19. Inu, Yehova, mukhala cikhalire,Ndi mpando wanu wacifumu ku mibadwo mibadwo.

20. Bwanji mutiiwala ciiwalire,Ndi kutisiya masiku ambirimbiri;

21. Mutitembenuzire kwa Inu, Yehova, ndipo tidzatembenuzidwadi,Mukonzenso masiku athu ngati kale lija.

22. Koma mwatikaniza konse,Mwatikwiyira kopambana.

Werengani mutu wathunthu Maliro 5