Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Malaki 4:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti taonani, likudza tsiku, lotentha ngati ng'anjo; ndipo onse akudzikuza ndi onse akucita coipa, adzakhala ngati ciputu; ndi tsiku lirinkudza lidzawayatsa, ati Yehova wa makamu, osawasiyira muzu kapena nthambi.

Werengani mutu wathunthu Malaki 4

Onani Malaki 4:1 nkhani