Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Malaki 3:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndidzadzudzula zolusa cifukwa ca inu, kuti zisakuonongereni zipatso za nthaka yanu; ngakhale mpesa wanu sudzayoyoka zipatso zace, zosaca m'munda, ati Yehova wa makamu.

Werengani mutu wathunthu Malaki 3

Onani Malaki 3:11 nkhani