Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Malaki 3:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mubwere nalo limodzi limodzi lonse la khumi, ku nyumba yosungiramo, kuti m'nyumba mwanga mukhale cakudya; ndipo mundiyese nako tsono, ati Yehova wa makamu, ngati sindikutsegulirani mazenera a kumwamba, ndi kukutsanulirani mdalitso wakuti adzasoweka malo akuulandira.

Werengani mutu wathunthu Malaki 3

Onani Malaki 3:10 nkhani