Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Malaki 2:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mukapanda kumvera, mukapanda kuliika mumtima mwanu, kupatsa dzina langa ulemerero, ati Yehova wa makamu, ndidzakutumizirani temberero, ndi kutemberera madalitso anu; inde, ndawatemberera kale cifukwa simuliika mumtima.

Werengani mutu wathunthu Malaki 2

Onani Malaki 2:2 nkhani