Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Malaki 1:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma wotembereredwa wonyengayo, wokhala nayo yaimuna m'gulu lace, nawinda, naphera Yehova nsembe cinthu cacirema; pakuti Ine ndine mfumu yaikuru, ati Yehova wa makamu; ndipo dzina langa ndi loopsa pakati pa amitundu.

Werengani mutu wathunthu Malaki 1

Onani Malaki 1:14 nkhani