Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Malaki 1:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mwenzi atakhala wina mwa inu wakutseka pamakomo, kuti musasonkhe moto cabe pa guwa langa la nsembe! Sindikondwera nanu, ati Yehova wa makamu, ndipo sindidzalandira capereka m'dzanja lanu.

Werengani mutu wathunthu Malaki 1

Onani Malaki 1:10 nkhani