Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 9:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nunene kwa ana a Israyeli, ndi kuti, Dzitengereni tonde akhale nsembe yaucimo; ndi mwana wa ng'ombe, ndi mwana wa nkhosa, a caka cimodzi, opanda cirema, akhale nsembe yopsereza;

Werengani mutu wathunthu Levitiko 9

Onani Levitiko 9:3 nkhani