Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 8:31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Mose anati kwa Aroni ndi kwa ana ace amuna, Phikani nyamayi pakhomo pa cihema cokomanako; ndipo muidyere komweko ndi mkate uli mu mtanga wa nsembe zodzaza manja, monga ndinauza, ndi kuti, Aroni ndi ana ace aidye.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 8

Onani Levitiko 8:31 nkhani