Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 23:40 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo tsiku loyambali mudzitengere nthambi za mitengo yokoma, nsomo za kanjedza, ndi nthambi za mitengo yobvalira, ndi misondodzi ya kumtsinje; ndipo mukondwere pamaso pa Yehova Mulungu wanu masiku asanu ndi awiri.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 23

Onani Levitiko 23:40 nkhani