Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 20:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti ali yense wakutemberera atate wace kapena mai wace azimupha ndithu; watemberera atate wace kapena mai wace; mwazi wace ukhale pamutu pace.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 20

Onani Levitiko 20:9 nkhani