Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 19:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Usamasautsa mnansi wako, kapena kulanda zace; mphotho yace ya wolipidwa isakhale ndi iwe kufikira m'mawa.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 19

Onani Levitiko 19:13 nkhani