Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 17:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo wansembeyo awaze mwaziwo pa guwa la nsembe la Yehova, pa khomo la cihema cokomanako, natenthe mafuta akhale pfungo lokoma lokwera kwa Yehova.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 17

Onani Levitiko 17:6 nkhani