Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 16:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo awazepo mwazi wina ndi cala cace kasanu ndi katatu; ndi kuliyeretsa ndi kulipatula kulicotsera zodetsa za ana a Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 16

Onani Levitiko 16:19 nkhani