Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 15:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo wakukhayo atayeretsedwa ku kukha kwace, adziwerengere masiku asanu ndi awiri akhale a kuyeretsa kwace, natsuke zobvala zace; nasambe thupi lace ndi madzi oyenda, nadzakhala woyera.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 15

Onani Levitiko 15:13 nkhani