Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 14:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo wansembe abviike cala cace ca dzanja lace lamanja ca iye mwini m'mafuta ali m'dzanja lace lamanzere, nawaze mafuta kasanu ndi kawiri ndi cala cace pamaso pa Yehova;

Werengani mutu wathunthu Levitiko 14

Onani Levitiko 14:16 nkhani