Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 12:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ici ndi cilamulo ca kwa iye wakubala, kapena mwana wamwamuna kapena wamkazi. Ndipo cuma cace cikapanda kufikira nkhosa, atenge njiwa ziwiri kapena maunda awiri; lina likhale nsembe yopsereza, ndi lina nsembe yaucimo; ndi wansembe amcitire comtetezera, ndipo adzakhalawoyera.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 12

Onani Levitiko 12:8 nkhani